Archive of all articles
There you can find all articles which are available in this language section of Botanix.
Category: Zonse Bowa Malangizo a kalimidwe ka mbewu Mapalmu Tizilombo towononga mbewu Udzu Zomera za chilendo Zomera za m’madzi
2012
November (1)2009
May (4)Gawo: Udzu
Udzu ungalimidwe ndi kusamaliridwa bwanji
Kodi mungatani ndi udzu / kapinga wotchetchedwa?
Ngati mumakonda kapinga wokongola, wamfupi ndi woyala bwino, muzitchetcha bwalo lanu mowilikiza. Panopa, udzu otchetchedwa pafupipafupi umabweretsa udzu wambiri umene umangokupatsa mavuto. Ndimangogwedeza mutu kusakhulupilira kuti anthu mosalabadira kuchotsa manyowa itchipitsitsa, otsika mtengo kwambiri.
Kodi mungatchetche bwanji bwalo lanu moyenera?
Kuli koyenera kutchetcha bwalo lanu moyenela kuti likhale ndi kapinga oyalana ndi odzadza bwino. Palibe mtengo wa conifer umene ungaoneke bwino utazunguliridwa ndi bwalo louma!
Musanatchetche bwalo, kumbukirani – udzu udulidwe mpaka kufika 1/3. Izi zikutanthauza kuti udzu kutali 6cm, ukuyenera kutchetchedwa kufika 4 cm. msinkhu wabwino wa udzu ndi 2–3 cm. ngati mukutchetcha pansi kwambiri, kapinga akhonza kuuma. Mukatha kutchetcha kapinga, muthilireni kwambiri (osachepera malita a madzi 10–15 pa sikweya mitala imodzi).
Kudzala kapinga watsopano
Nthawi yabwino yodzala kapinga kapena udzu owonjezera pa kapinga yemwe alipo kale ku Ulaya ndi kuchokera mwezi wa Meyi mpaka Juni. Julaye akhonza kukhala nthawi yabwino kudzala ngati kuli mvula.
Mbiri ya KPR

Gawani zomwe mukudziwa za kubyala mbewu komanso kusamalira zomera. Lembani nkhani zokhudza kubzyala ndi kusamalira mbewu komanso zomera, ndi zina zambiri, ndipo zisindikitseni muchinenero chanuchanu mu timabuku tathu ta Botanix! Lumikizanani nafe kuti mumve zambiri.
Category: Zonse Bowa Malangizo a kalimidwe ka mbewu Mapalmu Tizilombo towononga mbewu Udzu Zomera za chilendo Zomera za m’madzi